| Mulungu anatumiza aneneri kuti atiphunzitse mmene tingamupembedzere. |
| Ndipo mneneri aliyense ankatumizidwa ku gulu linalake la anthu |
| Mneneri akamwalira ndipo anthu ataya njira yowona |
| Mulungu amatumiza mneneri wina |
| Ndi zina zotero… |
| Aneneri onse adali kupitirizana wina ndi mzake ndipo adatumizidwa ndi uthenga womwewo (umene umaitanira Umodzi wa Mulungu (umadziwika mu Chiarabu kuti Allah)) |
| Mneneri aliyense anali njira yopita kwa Mulungu mu tsiku lake. |
| Abrahamu ndi Nowa anali njira kwa anthu awo m’nthawi yawo. |
| Momwemonso Yesu, Musa ndi Muhammad. |