| Mneneri womaliza kudza pambuyo pa Yesu adali Mtumiki Muhammad (SAW).
| Iye ndi Mneneri womaliza pa mndandanda wautali wa Aneneri amene adatumizidwa kuti adzaitane anthu kuti amvere ndi kupembedza Mulungu yekha (‘Allah’ m’Chiarabu). |
|---|
| Yesu ndi Muhammad (SAW) ndi akapolo ndi aneneri a Mulungu amene amatsogolera anthu kuti apembedze Allah. |
| Ndi nkhani ya nthawi |
| Ndipo Muhammad watumizidwa kwa anthu onse chifukwa iye ndi Mtumiki womaliza wa Mulungu. |
| Ngati muvomereza kuti Muhammadi ndi Mtumiki womaliza ndi kutsatira chiphunzitso chake, khulupirirani Yesu, Musa ndi aneneri onse. |
| 👉Sitimpembedza Muhammadi sitimpembedza Yesu, |
| Timangopembedza Mulungu Wamphamvuyonse amene adawalenga . |