Kodi mungayankhe mafunso awa musanakuonjezereni ku gulu lophunzirira 👇🏾
| 1️⃣ Yesu ndi ndani ? (a) Mulungu (b) Mwana wa Mulungu
| (c) Mneneri |
|---|
| 2️⃣ Muhammad ndi ndani ? |
| (a) Mneneri womaliza wa Mulungu. |
| (b) Sindikudziwa. |
| 3️⃣ Kodi buku lomaliza la Mulungu ndi liti ? |
| (a) Qur'an yopatulika |
| (b) Baibulo |
| (c) Sindikudziwa |